Apolisi ndi asilikali akupitilira kufufuza anthu amene anasowa pangozi ya boti pa Nyanja ya Kariba mdziko la Zimbabwe lachiwiri sabata yatha pamene chiwelengelo cha anthu omwalira chafika pa 92. John Kassim akulongosola zonse.

Anthu ena ku Malawi akufuna nthambi zina za boma zikhale zoyima pa zokha
05:30

Boma la Mozambique lakhwimitsa chitetezo cha mankhwala ndi makatemela
06:47

Linda Kasonde, Brebner Changala apeleka chikalata chotsutsa masankho a ku Zambia
06:32