Makhothi onse m’dziko la Zambia atsekedwa ndipo akuyang’aniridwa ndi asilikali, pomwe lero pa 24 August 2026 ndi tsiku lomaliza loti mtsogoleri wa Tonse Pamodzi Alliance, Brian Mundubile, apereke patition kapena kalata yotsutsa zotsatira za chisankho cha pa 13 August 2026. Zimenezi zachititsa kuti mabungwe angapo omenyera ufulu wa anthu atsutse zomwe boma lachita, ponena kuti kutsekedwa kwa makhothi komanso kuyang’aniridwa kwawo ndi asilikali ndikupondereza maufulu a anthu. Mada Phiri wamva zambiri kuchokela kwa Daniel Elisha Banda mtolankhani wa Channel Africa mdziko la Zambia.

Anthu ena ku Malawi akufuna nthambi zina za boma zikhale zoyima pa zokha
05:30

Boma la Mozambique lakhwimitsa chitetezo cha mankhwala ndi makatemela
06:47

Linda Kasonde, Brebner Changala apeleka chikalata chotsutsa masankho a ku Zambia
06:32