Anthu ena mdziko la Malawi akufuna kuti mabungwe ndi nthambi zina za boma zikhale zoyima pa zokha kuti boma lisamalowelere pa kagwilidwe ka ntchito zawo pamene ena akufuna kuti bungwe loyendetsa chisankho la MEC likhale loyima pa lokha. Jayne Chilimampunga wabwela ndi nkhani yonse

Boma la Mozambique lakhwimitsa chitetezo cha mankhwala ndi makatemela
06:47

Linda Kasonde, Brebner Changala apeleka chikalata chotsutsa masankho a ku Zambia
06:32

Akatswili pa nkhani ku Malawi akhumudwa ndi kubedwa kwa K700 miliyoni ku NOCMA
07:54