Ntchito yothandiza anamwino 500 a mdziko la Malawi kuti akagwile ntchito ku Israel chaka chino, yafika ku mapeto pamene mazana mazana anamwino omwe analamaliza maphunzilo awo sakugwila ntchito Ku Malawi. George Mhango wabwela ndi nkhani yonse

Anthu ena ku Malawi akufuna nthambi zina za boma zikhale zoyima pa zokha
05:30

Boma la Mozambique lakhwimitsa chitetezo cha mankhwala ndi makatemela
06:47

Linda Kasonde, Brebner Changala apeleka chikalata chotsutsa masankho a ku Zambia
06:32