Akatswiri omwe amayankhulapo zochitika zosiyana-siyana mdziko la Malawi, ati mzovetsa chisoni kuti adindo alephera kuteteza ndalama zomwe zabedwa ku company yowona za mafuta agalimoto ya NOCMA zokwana K700 million. Kondwani Nyamasauka ali ndi nkhani yonse.

Anthu ena ku Malawi akufuna nthambi zina za boma zikhale zoyima pa zokha
05:30

Boma la Mozambique lakhwimitsa chitetezo cha mankhwala ndi makatemela
06:47

Linda Kasonde, Brebner Changala apeleka chikalata chotsutsa masankho a ku Zambia
06:32