Mabungwe a matchalitchi ku Zambia adzudzula mawu a udani pa ndaleMabungwe atatu akuluakulu a mipingo m'dziko la Zambia, omwe ndi Zambia Conference of Catholic Bishops (ZCCB), Council of Churches in Zambia (CCZ), ndi Evangelical Fellowship of Zambia (EFZ), adzudzula kuchuluka kwa mawu oyambitsa mikangano, mawu achidani, kufalitsa nkhani za bodza komanso ziwawa zokhudzana ndi ndale pamene dzikolo likuyandikira chisankho cha patatu chomwe chidzachitike pa 13 August 2026. Daniel Elisha Banda ali ndi nkhani yonse.